Masalimo 148:4 - Buku Lopatulika4 Mlemekezeni, m'mwambamwamba, ndi madzi inu, a pamwamba pa thambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mlemekezeni, m'mwambamwamba, ndi madzi inu, a pamwamba pa thambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mtamandeni inu thambo lakumwambamwamba, ndi inu madzi a pamwamba pa thambo! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mutamandeni, inu thambo la kumwambamwamba ndi inu madzi a pamwamba pa thambo. Onani mutuwo |