Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 148:3 - Buku Lopatulika

3 Mlemekezeni, dzuwa ndi mwezi; mlemekezeni, nyenyezi zonse zounikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Mlemekezeni, dzuwa ndi mwezi; mlemekezeni, nyenyezi zonse zounikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mtamandeni inu dzuŵa ndi mwezi, mtamandeni inu nonse nyenyezi zoŵala!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Mutamandeni, inu dzuwa ndi mwezi, mutamandeni, inu nonse nyenyezi zowala.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 148:3
8 Mawu Ofanana  

Pakukhalabe masiku a dziko lapansi, nthawi yakubzala ndi yakukunkha, chisanu ndi mafundi, malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku sizidzalekai.


Pakuti Yehova atero: Ngati mukhoza kuswa pangano langa la usana ndi pangano langa la usiku, kuti usakhalenso usana ndi usiku, m'nyengo yao;


ndi kuti mungakweze maso anu kupenya kumwamba, ndipo poona dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi, khamu lonse la kumwamba, munganyengedwe ndi kuzigwadira, ndi kuzitumikira, zimene Yehova Mulungu wanu anagawira mitundu yonse ya anthu pansi pa thambo lonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa