Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 148:2 - Buku Lopatulika

2 Mlemekezeni, angelo ake onse; mlemekezeni, makamu ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Mlemekezeni, angelo ake onse; mlemekezeni, makamu ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mtamandeni inu angelo ake onse, mtamandeni inu magulu a ankhondo ake onse!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mutamandeni, inu angelo ake onse, mutamandeni, mutamandeni, inu zolengedwa za mmwamba.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 148:2
6 Mawu Ofanana  

Ndipo zinatha kupangidwa zakumwamba ndi dziko lapansi, ndi khamu lao lonse.


muja nyenyezi za m'mawa zinaimba limodzi mokondwera, ndi ana onse a Mulungu anafuula ndi chimwemwe?


Pamenepo mzimu unandinyamula, ndipo ndinamva kumbuyo kwanga mau a mkokomo waukulu, ndi kuti, Wodala ulemerero wa Yehova m'malo mwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa