Masalimo 148:1 - Buku Lopatulika1 Aleluya. Lemekezani Yehova kochokera kumwamba; mlemekezeni m'misanje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Aleluya. Lemekezani Yehova kochokera kumwamba; mlemekezeni m'misanje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tamandani Chauta! Tamandani Chauta inu okhala kumwamba, mtamandeni inu okhala mu mlengalenga! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tamandani Yehova. Tamandani Yehova, inu a kumwamba, mutamandeni Iye, inu a mlengalenga. Onani mutuwo |