Masalimo 103:20 - Buku Lopatulika20 Lemekezani Yehova, inu angelo ake; a mphamvu zolimba, akuchita mau ake, akumvera liu la mau ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Lemekezani Yehova, inu angelo ake; a mphamvu zolimba, akuchita mau ake, akumvera liu la mau ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tamandani Chauta, inu angelo ake, inu amphamvu amene mumamva mau ake, amene mumachita zimene amalamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tamandani Yehova, inu angelo ake, amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula, amene mumamvera mawu ake. Onani mutuwo |