Masalimo 148:6 - Buku Lopatulika6 Anazikhazikanso kunthawi za nthawi; anazipatsa chilamulo chosatumphika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Anazikhazikanso kunthawi za nthawi; anazipatsa chilamulo chosatumphika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adazikhazikitsa kuti zikhale mpaka muyaya, adaikapo lamulo limene silingathe kusinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye anaziyika pa malo ake ku nthawi za nthawi; analamula ndipo sizidzatha. Onani mutuwo |