Masalimo 95:5 - Buku Lopatulika5 Nyanja ndi yake, anailenga; ndipo manja ake anaumba dziko louma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nyanja ndi yake, anailenga; ndipo manja ake anaumba dziko louma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nyanja ndi yake, popeza kuti ndiye adailenga. Mtunda ndi wakenso, popeza kuti ndiye adaupanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Nyanja ndi yake, pakuti anayilenga ndi Iye, ndipo manja ake anawumba mtunda wowuma. Onani mutuwo |