Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 140:4 - Buku Lopatulika

Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Chauta, tetezeni kwa anthu oipa, tchinjirizeni kwa anthu andeu, amene amaganiza zofuna kundigwetsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa; tchinjirizeni kwa anthu ankhanza amene amakonza zokola mapazi anga.

Onani mutuwo



Masalimo 140:4
9 Mawu Ofanana  

M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Phazi la akudzikuza lisandifikire ine, ndi dzanja la oipa lisandichotse.


ukonda mau onse akuononga, lilime lachinyengo, iwe.


Imene siimvera liu la oitana, akuchita matsenga mochenjeratu.


Ndilanditseni, Mulungu wanga, m'dzanja la woipa, m'dzanja la munthu wosalungama ndi wachiwawa.


Kukometsa mlandu wa wamphulupulu mwatsankho sikuli kwabwino, ngakhale kuchitira chetera wolungama.