Masalimo 36:11 - Buku Lopatulika11 Phazi la akudzikuza lisandifikire ine, ndi dzanja la oipa lisandichotse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Phazi la akudzikuza lisandifikire ine, ndi dzanja la oipa lisandichotse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Musalole kuti mapazi a anthu odzikuza andipondereze, ndipo kuti manja a anthu oipa andipirikitse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane, kapena dzanja la oyipa kundithamangitsa. Onani mutuwo |