Masalimo 140:3 - Buku Lopatulika3 Anola lilime lao ngati njoka; pansi pa milomo yao pali ululu wa mphiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anola lilime lao ngati njoka; pansi pa milomo yao pali ululu wa mphiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Amanola lilime lao kuti likhale ngati la njoka, m'kamwa mwao muli ululu wa mamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iwo amanola malilime awo kukhala akuthwa ngati a njoka; pa milomo yawo pali ululu wa mamba. Sela Onani mutuwo |