Masalimo 140:2 - Buku Lopatulika2 amene adzipanga zoipa mumtima mwao; masiku onse amemeza nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 amene adzipanga zoipa mumtima mwao; masiku onse amemeza nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iwo amalingalira mumtima mwao kuti achite zoipa, amautsa nkhondo nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 amene mu mtima mwawo amakonza zinthu zoyipa ndi kuyambitsa nkhondo tsiku lililonse. Onani mutuwo |