Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 140:4 - Buku Lopatulika

4 Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Inu Chauta, tetezeni kwa anthu oipa, tchinjirizeni kwa anthu andeu, amene amaganiza zofuna kundigwetsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa; tchinjirizeni kwa anthu ankhanza amene amakonza zokola mapazi anga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 140:4
9 Mawu Ofanana  

M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Phazi la akudzikuza lisandifikire ine, ndi dzanja la oipa lisandichotse.


ukonda mau onse akuononga, lilime lachinyengo, iwe.


Imene siimvera liu la oitana, akuchita matsenga mochenjeratu.


Ndilanditseni, Mulungu wanga, m'dzanja la woipa, m'dzanja la munthu wosalungama ndi wachiwawa.


Kukometsa mlandu wa wamphulupulu mwatsankho sikuli kwabwino, ngakhale kuchitira chetera wolungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa