Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 71:4 - Buku Lopatulika

4 Ndilanditseni, Mulungu wanga, m'dzanja la woipa, m'dzanja la munthu wosalungama ndi wachiwawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndilanditseni, Mulungu wanga, m'dzanja la woipa, m'dzanja la munthu wosalungama ndi wachiwawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Landitseni Inu Mulungu wanga kwa anthu oipa, landitseni ku mphamvu za anthu osalungama ndi ankhalwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Landitseni Inu Mulungu wanga, kuchoka mʼdzanja la oyipa, kuchoka mʼdzanja la oyipa ndi anthu ankhanza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 71:4
9 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali, atapita iwo, ajawo anatuluka m'chitsime, nanka nauza mfumu Davide; nati kwa Davide, Nyamukani nimuoloke madzi msanga; pakuti Ahitofele anapangira zotere pa inu.


Ukani Yehova, Mumtsekereze, mumgwetse, landitsani moyo wanga kwa woipa ndi lupanga lanu;


Mundiweruzire, Mulungu, ndipo mundinenere mlandu kwa anthu opanda chifundo. Mundilanditse kwa munthu wonyenga ndi wosalungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa