Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 135:8 - Buku Lopatulika

Anapanda oyamba a Ejipito, kuyambira munthu kufikira zoweta.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anapanda oyamba a Ejipito, kuyambira munthu kufikira zoweta.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiye amene adapha ana achisamba a ku Ejipito, ana a anthu ndi a nyama omwe,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto, ana oyamba kubadwa a anthu ndi nyama.

Onani mutuwo



Masalimo 135:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anapha achisamba onse m'dziko mwao, choyambira cha mphamvu yao yonse.


Iye amene anapandira Aejipito ana ao oyamba; pakuti chifundo chake nchosatha.


Ndipo anapha ana oyamba onse a mu Ejipito, ndiwo oyamba a mphamvu yao m'mahema a Hamu.


Pakuti ndidzapita pakati padziko la Ejipito usiku womwewo, ndi kukantha ana oyamba onse m'dziko la Ejipito, anthu ndi zoweta; ndipo ndidzachita maweruzo pa milungu yonse ya Aejipito; Ine ndine Yehova.


ndipo kunakhala, pamene Farao anadziumitsa kuti tisamuke, Yehova anawapha onse oyamba kubadwa m'dziko la Ejipito, kuyambira oyamba a anthu, kufikira oyamba a zoweta; chifukwa chake ndimphera nsembe Yehova zazimuna zoyamba kubadwa zonse; koma oyamba onse a ana anga ndiwaombola.


Ndipo mtundu umene udzawayesa akapolo, ndidzauweruza Ine, anatero Mulungu; ndipo zitapita izi adzatuluka, nadzanditumikira Ine m'malo muno.