Masalimo 136:10 - Buku Lopatulika10 Iye amene anapandira Aejipito ana ao oyamba; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Iye amene anapandira Aejipito ana ao oyamba; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adapha ana achisamba a ku Ejipito, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |