Masalimo 135:9 - Buku Lopatulika9 Anatumiza zizindikiro ndi zodabwitsa pakati pako, Ejipito iwe, pa Farao ndi pa omtumikira onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anatumiza zizindikiro ndi zodabwitsa pakati pako, Ejipito iwe, pa Farao ndi pa omtumikira onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 amene adaonetsa Farao ndi atumiki ake onse zizindikiro zamphamvu ndi zodabwitsa m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye anatumiza zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa pakati pako, iwe Igupto, kutsutsana ndi Farao pamodzi ndi atumiki ake onse. Onani mutuwo |