Masalimo 135:10 - Buku Lopatulika10 Ndiye amene anapanda amitundu ambiri, napha mafumu amphamvu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndiye amene anapanda amitundu ambiri, napha mafumu amphamvu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndiye amene adaononga mitundu yambiri ya anthu, ndi kupha mafumu amphamvu aja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iye anakantha mitundu yambiri ya anthu ndi kupha mafumu amphamvu: Onani mutuwo |