Masalimo 135:8 - Buku Lopatulika8 Anapanda oyamba a Ejipito, kuyambira munthu kufikira zoweta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Anapanda oyamba a Ejipito, kuyambira munthu kufikira zoweta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndiye amene adapha ana achisamba a ku Ejipito, ana a anthu ndi a nyama omwe, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto, ana oyamba kubadwa a anthu ndi nyama. Onani mutuwo |