Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:4 - Buku Lopatulika

Anene tsono iwo akuopa Yehova, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anene tsono iwo akuopa Yehova, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu oopa Chauta anene kuti, “Chikondi chake nchamuyaya.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo amene amaopa Yehova anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”

Onani mutuwo



Masalimo 118:4
5 Mawu Ofanana  

Pakuti Yehova ndiye wabwino; chifundo chake chimanka muyaya; ndi chikhulupiriko chake ku mibadwomibadwo.


Israele, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao ndi chikopa chao.


Yamikani Yehova, pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake nchosatha.


Inu akuopa Yehova, mumlemekeze; inu nonse mbumba ya Yakobo, mumchitire ulemu; ndipo muchite mantha ndi Iye, inu nonse mbumba ya Israele.


Ndipo mau anachokera kumpando wachifumu, ndi kunena, Lemekezani Mulungu wathu akapolo ake onse akumuopa Iye, aang'ono ndi aakulu.