Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:3 - Buku Lopatulika

3 Anene tsono nyumba ya Aroni, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Anene tsono nyumba ya Aroni, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Banja la Aroni linene kuti, “Chikondi chake nchamuyaya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Banja la Aaroni linene kuti, “Chikondi chake ndi chosatha.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:3
6 Mawu Ofanana  

Nyumba ya Aroni, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao, ndi chikopa chao.


inunso ngati miyala yamoyo mumangidwa nyumba ya uzimu, kuti mukhale ansembe oyera mtima, akupereka nsembe zauzimu, zolandiridwa ndi Mulungu mwa Yesu Khristu.


natiyesa ife ufumu tikhale ansembe a Mulungu ndiye Atate wake; kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu kufikira nthawi za nthawi. Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa