Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:2 - Buku Lopatulika

2 Anene tsono Israele, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Anene tsono Israele, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Aisraele anene kuti, “Chikondi chake nchamuyaya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Israeli anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:2
7 Mawu Ofanana  

Ntchito zanu zonse zidzakuyamikani, Yehova; ndi okondedwa anu adzakulemekezani.


Ndipo onse amene atsata chilangizo ichi, mtendere ndi chifundo zikhale pa iwo, ndi pa Israele wa Mulungu.


Potero mwa Iye tipereke chiperekere nsembe yakuyamika Mulungu, ndiyo chipatso cha milomo yovomereza dzina lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa