Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:4 - Buku Lopatulika

4 Anene tsono iwo akuopa Yehova, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Anene tsono iwo akuopa Yehova, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Anthu oopa Chauta anene kuti, “Chikondi chake nchamuyaya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Iwo amene amaopa Yehova anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:4
5 Mawu Ofanana  

Pakuti Yehova ndiye wabwino; chifundo chake chimanka muyaya; ndi chikhulupiriko chake ku mibadwomibadwo.


Israele, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao ndi chikopa chao.


Yamikani Yehova, pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake nchosatha.


Inu akuopa Yehova, mumlemekeze; inu nonse mbumba ya Yakobo, mumchitire ulemu; ndipo muchite mantha ndi Iye, inu nonse mbumba ya Israele.


Ndipo mau anachokera kumpando wachifumu, ndi kunena, Lemekezani Mulungu wathu akapolo ake onse akumuopa Iye, aang'ono ndi aakulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa