Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:5 - Buku Lopatulika

5 M'mene ndinasautsika ndinaitanira pa Yehova; anandiyankha nandiika motakasuka Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 M'mene ndinasautsika ndinaitanira pa Yehova; anandiyankha nandiika motakasuka Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Pamene ndinali m'mavuto ndidapemphera kwa Chauta, ndipo Iye adandichotsera mavutowo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova, ndipo Iye anayankha pondichotsa mʼmasautsowo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:5
15 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anaopa kwambiri, navutidwa; ndipo anagawa anthu anali nao ndi nkhosa ndi zoweta, ndi ngamira, zikhale makamu awiri;


Pamenepo anafuulira kwa Yehova mumsauko mwao, ndipo anawapulumutsa m'kupsinjika kwao.


Pamenepo afuulira kwa Yehova m'kusauka kwao, ndipo awapulumutsa m'kupsinjika kwao.


Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza.


Ananditulutsanso andifikitse motakasuka; anandilanditsa, pakuti anakondwera ndi ine.


Yehova anandibwezera monga mwa chilungamo changa; anandisudzula monga mwa kusisira kwa manja anga.


M'kusauka kwanga ndinaitana Yehova, ndipo ndinakuwira Mulungu wanga; mau anga anawamva mu Kachisi mwake, ndipo mkuwo wanga wa pankhope pake unalowa m'makutu mwake.


Ndipo simunandipereke m'dzanja la mdani; munapondetsa mapazi anga pali malo.


Tsiku la nsautso yanga ndinafuna Ambuye. Dzanja langa linatambalika usiku, losaleka; mtima wanga unakana kutonthozedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa