Masalimo 118:6 - Buku Lopatulika6 Yehova ndi wanga; sindidzaopa; adzandichitanji munthu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Yehova ndi wanga; sindidzaopa; adzandichitanji munthu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chauta akakhala pa mbali yanga, sindichita mantha. Munthu angandichite chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova ali nane; sindidzachita mantha. Munthu angandichite chiyani? Onani mutuwo |