Masalimo 118:7 - Buku Lopatulika7 Yehova ndi wanga, mwa iwo akundithandiza; m'mwemo ndidzaona chofuna ine pa iwo akundida. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Yehova ndi wanga, mwa iwo akundithandiza; m'mwemo ndidzaona chofuna ine pa iwo akundida. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chauta ali pa mbali yanga kuti andithandize. Odana nane ndidzaŵayang'ana monyoza nditaŵapambana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa. Ndidzayangʼana adani anga mwachipambano. Onani mutuwo |