Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 102:9 - Buku Lopatulika

Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusakaniza chomwera changa ndi misozi,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusanganiza chomwera changa ndi misozi,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inetu ndimadya phulusa ngati chakudya, chakumwa changa ndimasakaniza ndi misozi,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti ndimadya phulusa ngati chakudya changa ndi kusakaniza chakumwa changa ndi misozi

Onani mutuwo



Masalimo 102:9
10 Mawu Ofanana  

Pakuti ndikati ndidye, kumadza kuusa moyo kwanga; ndi kudzuma kwanga kumathiridwa ngati madzi.


Udziweramiranji moyo wanga iwe? Ndi kuzingwa m'kati mwanga? Yembekeza Mulungu; pakuti ndidzamlemekeza tsopanonso, ndiye chipulumutso cha nkhope yanga ndi Mulungu wanga.


Misozi yanga yakhala ngati chakudya changa, usana ndi usiku; pakunena iwo kwa ine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?


Ndipo anandipatsa ndulu ikhale chakudya changa; nandimwetsa vinyo wosasa pomva ludzu ine.


Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri.


Iye adya phulusa; mtima wodzinyenga wampambutsa, kuti iye sangapulumutse moyo wake, pena kunena, Kodi simuli kunama m'dzanja langa lamanja?


Musachifotokoza mu Gati, musalira misozi konse; m'nyumba ya Afira ndinagubuduka m'fumbi.


Adzanyambita fumbi ngati njoka; ngati zokwawa za padziko, adzanjenjemera potuluka m'ngaka mwao; adzafika kwa Yehova Mulungu wao ndi mantha, nadzaopa chifukwa cha iwe.