Masalimo 102:10 - Buku Lopatulika10 chifukwa cha ukali wanu ndi kuzaza kwanu; popeza munandinyamula ndipo munandigwetsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 chifukwa cha ukali wanu ndi kuzaza kwanu; popeza munandinyamula ndipo munandigwetsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 chifukwa cha ukali wanu ndi mkwiyo wanu, popeza kuti Inu mwandinyamula ndi kunditaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 chifukwa cha ukali wanu waukulu, popeza Inu mwandinyamula ndi kunditayira kumbali. Onani mutuwo |