Masalimo 102:11 - Buku Lopatulika11 Masiku anga akunga mthunzi womka m'tali; ndipo ine ndauma ngati udzu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Masiku anga akunga mthunzi womka m'tali; ndipo ine ndauma ngati udzu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Masiku anga ali pafupi kutha ngati mthunzi wamadzulo. Ndikufota ngati udzu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Masiku anga ali ngati mthunzi wa kumadzulo; Ine ndikufota ngati udzu. Onani mutuwo |