Masalimo 102:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusakaniza chomwera changa ndi misozi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusanganiza chomwera changa ndi misozi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Inetu ndimadya phulusa ngati chakudya, chakumwa changa ndimasakaniza ndi misozi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pakuti ndimadya phulusa ngati chakudya changa ndi kusakaniza chakumwa changa ndi misozi Onani mutuwo |