Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 102:8 - Buku Lopatulika

8 Adani anga anditonza tsiku lonse; akundiyalukirawo alumbirira ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Adani anga anditonza tsiku lonse; akundiyalukirawo alumbirira ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsiku lonse adani anga amandichita chipongwe, onse ondinyoza amatchula dzina langa potemberera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Tsiku lonse adani anga amandichita chipongwe; iwo amene amandinyoza, amagwiritsa ntchito dzina langa ngati temberero.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 102:8
15 Mawu Ofanana  

Aphokoseranji amitundu, nalingiriranji anthu zopanda pake?


Adani anga andinenera choipa, ndi kuti, adzafa liti, ndi kutayika dzina lake?


chifukwa cha mau a mdani, chifukwa cha kundipsinja woipa; pakuti andisenza zopanda pake, ndipo adana nane mumkwiyo.


Chotonza chandiswera mtima, ndipo ndidwala ine; ndipo ndinayembekeza wina wondichitira chifundo, koma palibe; ndinayembekeza onditonthoza mtima, osawapeza.


Ndinaganizira masiku akale, zaka zakalekale.


Chimene adani anu, Yehova, atonza nacho; chimene atonzera nacho mayendedwe a wodzozedwa wanu.


Ndipo mudzasiya dzina lanu likhale chitemberero kwa osankhidwa anga, ndipo Ambuye Yehova adzakupha iwe, nadzatcha atumiki ake dzina lina;


ndipo am'nsinga onse a Yuda amene ali mu Babiloni adzatemberera pali iwo, kuti, Yehova akuchitire iwe monga Zedekiya ndi Ahabu, amene mfumu ya ku Babiloni inaotcha m'moto;


Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzake kuti amchitire Yesu chiyani.


Ndipo ndinawalanga kawirikawiri m'masunagoge onse, ndi kuwakakamiza anene zamwano; ndipo pakupsa mtima kwakukulu pa iwo ndinawalondalonda ndi kuwatsata ngakhale kufikira kumizinda yakunja.


Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano.


Pakuti Khristunso sanadzikondweretse yekha; koma monga kwalembedwa, Minyozo ya iwo amene anakunyoza iwe inagwa pa Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa