Masalimo 102:7 - Buku Lopatulika7 Ndidikira, ndikhala ngati mbalame ili yokha pamwamba pa tsindwi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndidikira, ndikhala ngati mbalame ili yokha pamwamba pa tsindwi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndimagona osapeza tulo, ndili ngati mbalame yokhala yokha pa denga, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndimagona osapeza tulo; ndakhala ngati mbalame yokhala yokha pa denga. Onani mutuwo |