Mika 7:17 - Buku Lopatulika17 Adzanyambita fumbi ngati njoka; ngati zokwawa za padziko, adzanjenjemera potuluka m'ngaka mwao; adzafika kwa Yehova Mulungu wao ndi mantha, nadzaopa chifukwa cha iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Adzanyambita fumbi ngati njoka; ngati zokwawa za padziko, adzanjenjemera potuluka m'ngaka mwao; adzafika kwa Yehova Mulungu wao ndi mantha, nadzaopa chifukwa cha iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Adzavimvinizika pa dothi ngati njoka, ngati zolengedwa zina zokwaŵa. Adzabwera ali njenjenje kuchokera ku malinga ao. Moopa adzatembenukira kwa Inu Chauta, Mulungu wathu, ndipo adzachita nanu mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Adzabwira fumbi ngati njoka, ngati zolengedwa zomwe zimakwawa pansi. Adzabwera akunjenjemera kuchokera mʼmaenje awo; mwamantha adzatembenukira kwa Yehova Mulungu wathu ndipo adzachita nanu mantha. Onani mutuwo |