Mika 7:16 - Buku Lopatulika16 Amitundu adzaona nadzachita manyazi ndi mphamvu yao yonse; adzagwira pakamwa, m'makutu mwao mudzagontha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Amitundu adzaona nadzachita manyazi ndi mphamvu yao yonse; adzagwira pakamwa, m'makutu mwao mudzagontha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Anthu a mitundu yambiri akadzaona zimenezo adzachita manyazi, ngakhale ali ndi mphamvu zotani. Adzangogwira pakamwa, ndi kutseka makutu motaya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Mitundu ya anthu idzaona zimenezi ndipo idzachita manyazi, ngakhale ali ndi mphamvu zotani. Adzagwira pakamwa pawo ndipo makutu awo adzagontha. Onani mutuwo |