Mika 7:15 - Buku Lopatulika15 Monga masiku a kutuluka kwako m'dziko la Ejipito ndidzamuonetsa zodabwitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Monga masiku a kutuluka kwako m'dziko la Ejipito ndidzamuonetsa zodabwitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Chauta akuti, “Ndidzaŵaonetsa zodabwitsa, monga masiku amene ankatuluka ku Ejipito.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Ndidzawaonetsa zodabwitsa zanga, ngati masiku amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto.” Onani mutuwo |