Mika 1:10 - Buku Lopatulika10 Musachifotokoza mu Gati, musalira misozi konse; m'nyumba ya Afira ndinagubuduka m'fumbi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Musachifotokoza m'Gati, musalira misozi konse; m'nyumba ya Afira ndinagubuduka m'fumbi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Musaŵauze zimenezi a ku Gati, musalire konse. Muvimvinizike m'fumbi ku Beteleafura, kuwonetsa chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Musanene zimenezi ku Gati; musalire nʼkomwe. Mugubuduzike mu fumbi ku Beti-Leafura. Onani mutuwo |