Mika 1:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti mabala ake ndi osapola; pakuti afikira ku Yuda; afikira ku chipata cha anthu anga, ku Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti mabala ake ndi osapola; pakuti afikira ku Yuda; afikira ku chipata cha anthu anga, ku Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Samariya, zilonda za uchimo wake sizingathe kupola, zafika mpaka ku Yuda. Chiwonongeko chili pafupi ndi mzinda wa anthu anga, chafika mpaka ku Yerusalemu kwenikweni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pakuti chilonda cha Samariya nʼchosachizika; chafika ku Yuda. Chafika pa chipata chenicheni cha anthu anga, mpaka mu Yerusalemu mwenimwenimo. Onani mutuwo |