Mika 1:8 - Buku Lopatulika8 Chifukwa cha ichi ndidzachita maliro, ndi kuchema, ndidzayenda wolandidwa ndi wamaliseche; ndidzalira ngati nkhandwe, ndi kubuma ngati nthiwatiwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chifukwa cha ichi ndidzachita maliro, ndi kuchema, ndidzayenda wolandidwa ndi wamaliseche; ndidzalira ngati nkhandwe, ndi kubuma ngati nthiwatiwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono Mika adati, “Nchifukwa chake ndidzalira komvetsa chisoni. Ndidzayenda maliseche, ndidzakuwa ngati nkhandwe ndi kulira ngati nthiŵatiŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Chifukwa cha zimenezi ine ndidzalira momvetsa chisoni; ndidzayenda wopanda nsapato ndi wamaliseche. Ndidzafuwula ngati nkhandwe ndi kulira ngati kadzidzi. Onani mutuwo |