Masalimo 69:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo anandipatsa ndulu ikhale chakudya changa; nandimwetsa vinyo wosasa pomva ludzu ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo anandipatsa ndulu ikhale chakudya changa; nandimwetsa vinyo wosasa pomva ludzu ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Adandipatsa ulembe kuti ndidye, ndipo nditamva ludzu, adandipatsa vinyo wosasa kuti ndimwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Iwo anayika ndulu mʼchakudya changa ndi kundipatsa vinyo wosasa chifukwa cha ludzu. Onani mutuwo |