Masalimo 69:20 - Buku Lopatulika20 Chotonza chandiswera mtima, ndipo ndidwala ine; ndipo ndinayembekeza wina wondichitira chifundo, koma palibe; ndinayembekeza onditonthoza mtima, osawapeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Chotonza chandiswera mtima, ndipo ndidwala ine; ndipo ndinayembekeza wina wondichitira chifundo, koma palibe; ndinayembekeza onditonthoza mtima, osawapeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Mtima wanga wasweka chifukwa cha zipongwe, ndataya mtima kotheratu. Ndidafunafuna ena ondichitira chifundo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe. Ndidafunafunanso ena ondisangalatsa, koma sindidampeze ndi mmodzi yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mnyozo waswa mtima wanga ndipo wandisiya wopanda thandizo lililonse; ndinafunafuna ena woti andichitire chisoni, koma panalibe ndi mmodzi yemwe woti anditonthoze, sindinapeze ndi mmodzi yemwe. Onani mutuwo |