Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 80:5 - Buku Lopatulika

5 Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mwaŵadyetsa chisoni ngati chakudya, mwaŵapatsa misozi ngati chakumwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mwawadyetsa buledi wa misozi; mwachitisa iwo kumwa misozi yodzaza mbale.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:5
9 Mawu Ofanana  

Zimene moyo wanga ukana kuzikhudza zikunga chakudya chosakolera kwa ine.


Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusakaniza chomwera changa ndi misozi,


Misozi yanga yakhala ngati chakudya changa, usana ndi usiku; pakunena iwo kwa ine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?


Mulungu, munatitayiranji chitayire? Mkwiyo wanu ufukiranji pa nkhosa za kubusa kwanu?


Yehova, mudzakwiya nthawi zonse kufikira liti? Nidzatentha nsanje yanu ngati moto?


Ndipo ngakhale Ambuye adzakupatsani inu chakudya cha nsautso, ndi madzi a chipsinjo, koma aphunzitsi ako sadzabisikanso, koma maso ako adzaona aphunzitsi ako;


Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola, mwatipha osachitira chisoni.


Mwadzikuta ndi mtambo kuti pemphero lathu lisapyolemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa