Masalimo 80:5 - Buku Lopatulika5 Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mwaŵadyetsa chisoni ngati chakudya, mwaŵapatsa misozi ngati chakumwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mwawadyetsa buledi wa misozi; mwachitisa iwo kumwa misozi yodzaza mbale. Onani mutuwo |