Masalimo 80:4 - Buku Lopatulika4 Yehova, Mulungu wa makamu, mudzakwiyira pemphero la anthu anu kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Yehova, Mulungu wa makamu, mudzakwiyira pemphero la anthu anu kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Inu Chauta, Mulungu Wamphamvuzonse, mudzakwiyira mapemphero a anthu anu mpaka liti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Inu Mulungu Wamphamvuzonse, mpaka liti mkwiyo wanu udzanyeka kutsutsana ndi mapemphero a anthu anu? Onani mutuwo |