Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 80:4 - Buku Lopatulika

4 Yehova, Mulungu wa makamu, mudzakwiyira pemphero la anthu anu kufikira liti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Yehova, Mulungu wa makamu, mudzakwiyira pemphero la anthu anu kufikira liti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Inu Chauta, Mulungu Wamphamvuzonse, mudzakwiyira mapemphero a anthu anu mpaka liti?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Inu Mulungu Wamphamvuzonse, mpaka liti mkwiyo wanu udzanyeka kutsutsana ndi mapemphero a anthu anu?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:4
14 Mawu Ofanana  

Yehova, musandichititse manyazi; pakuti ndafuulira kwa Inu, oipa achite manyazi, atonthole m'manda.


Mwapatsa chimwemwe mumtima mwanga, chakuposa chao m'nyengo yakuchuluka dzinthu zao ndi vinyo wao.


Ndinu Yehova, Mulungu wa makamu, Mulungu wa Israele. Ukani kukazonda amitundu onse, musachitire chifundo mmodzi yense wakuchita zopanda pake monyenga.


Mwaonetsa anthu anu zowawa, mwatimwetsa vinyo wotinjenjemeretsa.


Mulungu, munatitayiranji chitayire? Mkwiyo wanu ufukiranji pa nkhosa za kubusa kwanu?


Yehova, mudzakwiya nthawi zonse kufikira liti? Nidzatentha nsanje yanu ngati moto?


Kodi mudzatikwiyira nthawi zonse? Kodi mudzakhala chikwiyire mibadwomibadwo?


Mwadzikuta ndi mtambo kuti pemphero lathu lisapyolemo.


Ndipo tsopano, Mulungu wathu, mumvere pemphero la mtumiki wanu, ndi mapembedzero ake, nimuwalitse nkhope yanu pamalo anu opatulika amene ali opasuka, chifukwa cha Ambuye.


Yehova sadzamkhululukira, koma pamenepo mkwiyo wa Yehova ndi nsanje yake zidzamfukira munthuyo; ndipo temberero lonse lolembedwa m'buku ili lidzamkhalira; ndipo Yehova adzafafaniza dzina lake pansi pa thambo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa