Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 80:3 - Buku Lopatulika

3 Mutibweze, Mulungu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Mutibweze, Mulungu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Inu Mulungu, tibwezereni mwakale, mutiwonetse nkhope yanu yokondwa, ndipo ife tidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Tibwezereni mwakale Inu Mulungu; nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:3
12 Mawu Ofanana  

Ndimvereni Yehova, ndimvereni, kuti anthu awa adziwe kuti Inu Yehova ndinu Mulungu, ndi kuti Inu mwabwezanso mitima yao.


Muwalitse nkhope yanu pa mtumiki wanu; ndipo mundiphunzitse malemba anu.


Ambiri amati, Adzationetsa chabwino ndani? Weramutsirani ife kuunika kwa nkhope yanu, Yehova.


Mwatitaya Mulungu, mwatipasula; mwakwiya; tibwezereni.


Atichitire chifundo Mulungu, ndi kutidalitsa, atiwalitsire nkhope yake;


Mbusa wa Israele, tcherani khutu; inu wakutsogolera Yosefe ngati nkhosa; inu wokhala pa akerubi, walitsani.


Mutibweze, Yehova Mulungu wa makamu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.


Mulungu wa makamu, mutibweze; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.


Mutibweze, Mulungu wa chipulumutso chathu, nimuletse udani wanu wa pa ife.


Mutitembenuzire kwa Inu, Yehova, ndipo tidzatembenuzidwadi, mukonzenso masiku athu ngati kale lija.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa