Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 102:7 - Buku Lopatulika

Ndidikira, ndikhala ngati mbalame ili yokha pamwamba pa tsindwi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndidikira, ndikhala ngati mbalame ili yokha pamwamba pa tsindwi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndimagona osapeza tulo, ndili ngati mbalame yokhala yokha pa denga,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndimagona osapeza tulo; ndakhala ngati mbalame yokhala yokha pa denga.

Onani mutuwo



Masalimo 102:7
9 Mawu Ofanana  

Ndili mbale wao wa ankhandwe, ndi mnansi wao wa nthiwatiwa.


Moyo wanga uyang'anira Ambuye, koposa alonda matanda kucha; inde koposa alonda matanda kucha.


Mulungu wanga, ndiitana usana, koma simuvomereza; ndipo usiku, sindikhala chete.


Ondikonda ndi anzanga apewa mliri wanga; ndipo anansi anga aima patali.


Mundikhalitsa maso; ndigwidwa mtima wosanena kanthu.