Masalimo 38:11 - Buku Lopatulika11 Ondikonda ndi anzanga apewa mliri wanga; ndipo anansi anga aima patali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ondikonda ndi anzanga apewa mliri wanga; ndipo anansi anga aima patali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Abwenzi anga ndi anzanga omwe amandiimira kutali, chifukwa cha matenda anga. Achibale anga nawonso amandipewa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga; anansi anga akhala kutali nane. Onani mutuwo |