Masalimo 38:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anditchera misampha iwo akufuna moyo wanga; ndipo iwo akuyesa kundichitira choipa alankhula zoononga, nalingirira zonyenga tsiku lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anditchera misampha iwo akufuna moyo wanga; ndipo iwo akuyesa kundichitira choipa alankhula zoononga, nalingirira zonyenga tsiku lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu ofunafuna moyo wanga, amanditchera misampha. Ofuna kundipweteka amalankhula zondiwononga, tsiku lonse amangolingalira zondichita chiwembu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo, oti andipwetekewo amayankhula za kuwonongeka kwanga; tsiku lonse amakonza zachinyengo. Onani mutuwo |