Masalimo 38:13 - Buku Lopatulika13 Koma ine, monga gonthi, sindimva; ndipo monga munthu wosalankhula, sinditsegula pakamwa panga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma ine, monga gonthi, sindimva; ndipo monga munthu wosalankhula, sinditsegula pakamwa panga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma ine ndili ngati gonthi, sindikumvako, ndili ngati mbeŵeŵe amene satha kulankhula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve, monga wosayankhula, amene sangathe kutsekula pakamwa pake; Onani mutuwo |