Masalimo 38:14 - Buku Lopatulika14 Inde ndikunga munthu wosamva, ndipo m'kamwa mwanga mulibe makani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Inde ndikunga munthu wosamva, ndipo m'kamwa mwanga mulibe makani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Inde ndili ngati munthu amene saamva, chifukwa sindingathe kuyankhapo kanthu, pamene akundilankhula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndakhala ngati munthu amene samva, amene pakamwa pake sipangathe kuyankha. Onani mutuwo |