Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 130:6 - Buku Lopatulika

6 Moyo wanga uyang'anira Ambuye, koposa alonda matanda kucha; inde koposa alonda matanda kucha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Moyo wanga uyang'anira Ambuye, koposa alonda matanda kucha; inde koposa alonda matanda kucha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Mtima wanga umayembekeza Chauta kupambana m'mene alonda amayembekezera mbandakucha, kupambanadi m'mene alonda amayembekezera mbandakucha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Moyo wanga umayembekezera Ambuye, kupambana momwe alonda amayembekezera mmawa, inde, kupambana momwe alonda amayembekezera mmawa,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 130:6
6 Mawu Ofanana  

Ndinafuula kusanake: ndinayembekezera mau anu.


Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse, akuimirira m'nyumba ya Yehova usiku.


Ndipulumutseni kwa zolakwa zanga zonse, musandiike ndikhale chotonza cha wopusa.


Pokumbukira Inu pa kama wanga, ndi kulingalira za Inu maulonda a usiku.


Ndipo iye anafuulitsa ngati mkango, Ambuye inu, ine ndiimabe pamwamba pa nsanja nthawi ya usana, ndipo ndiikidwa mu ulonda wanga usiku wonse;


Ndipo pakuopa tingatayike pamiyala, anaponya anangula anai kumakaliro, nakhumba kuti kuche.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa