Masalimo 22:2 - Buku Lopatulika2 Mulungu wanga, ndiitana usana, koma simuvomereza; ndipo usiku, sindikhala chete. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mulungu wanga, ndiitana usana, koma simuvomereza; ndipo usiku, sindikhala chete. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mulungu wanga, ine ndimalira usana, koma Inu simundiyankha, ndimalira usiku, koma sindipeza mpumulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu Mulungu wanga, ine ndimalira masana, koma simuyankha, usikunso, ndipo sindikhala chete. Onani mutuwo |