Masalimo 22:3 - Buku Lopatulika3 Koma Inu ndinu woyera, wakukhala m'malemekezo a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma Inu ndinu woyera, wakukhala m'malemekezo a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Komabe Inu ndinu oyera, mumakhala pa mpando wanu waufumu, ndipo anthu anu Aisraele amakutamandani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inu ndinu Woyera, wokhala pa mpando waufumu; ndinu matamando a Israeli. Onani mutuwo |